18 "Mzimu wa Ambuye uli mkati mwanga,
pakuti wanisangha
kwaakambila wosauka uthenga wabwino.
Anituma kuti nauzile wandhu womangidwa ufulu wao,
ni wosapenya akhoze kuonanjho,
ni kwaapacha ufulu yawo aoneledwa.
19 Ni kuuzila chaka cha Ambuye icho chavomelezedwa."