Pular para o conteúdo
Publicidade

Lucas 4

18 "Mzimu wa Ambuye uli mkati mwanga,

pakuti wanisangha

kwaakambila wosauka uthenga wabwino.

Anituma kuti nauzile wandhu womangidwa ufulu wao,

ni wosapenya akhoze kuonanjho,

ni kwaapacha ufulu yawo aoneledwa.

19 Ni kuuzila chaka cha Ambuye icho chavomelezedwa."

Veja também