Pular para o conteúdo
Publicidade

Lucas 5

Yesu wafunjhidwa nghani zomanga kudya

33 Wandhu wina adamkambila, "Oyaluzidwa a Yohana mbatizi atomanga kudya ni kupembhela ndhawi zonjhe, ni oyaluzidwa a Mafalisayo achita chimwecho. Nambho oyaluzidwa wako angokudya ni kumwa." 34 Yesu wadaayangha, "Bwanji, mganiza mkhoza kwachita alendo amwene ukwati kumanga kudya ndhawi iyo ali ni iye mwenewake? 35 Nambho nyengo itokujha yapo mwene ukwati siwatengedwe pakati pawo, pamenepo nde yapo samange kudya."

Veja também