Pular para o conteúdo
Publicidade

Lucas 8

2 Ni wachikazi wina adachochedwa viwanda, ni kwalamicha matenda yawo, adapiata pamojhi ni iye. Wachikaziwo adali, Maliya kuchokela ku Magedelena, uyo wadachochedwa viwanda saba, 3 Ni Yoane mkazake wa Kuza, wamkulu wa alonda wa nyumba ya Helode, Susana ni wina ambili. Wachikazi anyiyawa amamthangatila Yesu pamojhi ni oyaluzidwa wake kwa chuma chao achinawenewake.

Veja também