Yao afunika kukhala oyaluzidwa a Yesu
57 Yapo adali mnjila, mundhu mmojhi wadamkambila Yesu, "Sinikuchateni kulikonjhe uko simupite." 58 Yesu wadayangha, "Nghandwe zili ni mbhanga, ni mbalame za kumlengalenga zili ni visa, nambho mwana wa mundhu walibe pa malo pogona ni kupumulila."
59 Ndiipo, wadamkambila mundhu mwina, "Nichate." Nambho mundhu yujha wadayangha, "Ambuye, munisiye uti nipite nikaazike atate wanga." 60 Nambho Yesu wadamkambila, "Asiye wandhu akufa waazike akufa anjao, nambho iwe pita ukaulalikile Ufumu wa Mnungu."
61 Mundhu mwina wadamkambila Yesu, "Ambuye, sinikuchateni, nambho munilole uti nipite nikalaile wandhu a kukhom langa." 62 Yesu wadamkambila, "Palibe mundhu uyo wagwila khasu ni kuyamba kulima wapenyanjho mmbuyo, mundhu mmeneyo siwafunika kulowa mu Ufumu wa Mnungu."