Achabale ni amae auzene a Yesu
46 Yesu yapo wadali wakali kukambana ni gulu la wandhu, maye wake ni achabale wake adajha ni kuima kubwalo, naafuna kukamba nayo. 47 Ndiipo mundhu mmojhi wadamkambila, "Maye wako ni achabale wako ali kubwalo, afuna kukambana ni iwe."
48 Yesu wadamuyangha mundhuyo, "Maye wanga ni ayani? Ni achabale wanga ni achiyani?" 49 Ndiipo wadatambasulila jhanja lake ni kwaalangizila oyaluzidwa wake, ni wakamba, "Anyiyawa nde maye wanga ni achabale wanga! 50 Walionjhe uyo wachita vijha avifuna Atate wanga ali kumwamba, mmeneyo nde mbale wanga, ni mlongo wanga ni maye wanga."