Pular para o conteúdo
Publicidade

Mateus 25

35 Nidali ni njala mdanipacha chakudya, ni nidali nilujho mdanipacha majhi ya kumwa, ni nidali mlendo mdanilandila mnyumba zanu. 36 Nidalibe njhalu mdaniveka, nidali odwala mdanidwaza ni nidali mndende mdaniyendela.37 Pamenepo wandhu abwino siamuyanghe Mbuye, Liti tidakuonani muli ninjala tidakupachani chakudya ni liti mudali ni lujho tidakupachani majhi ya kumwa? 38 Liti tidakuonani mwali alendo niife kukulandilani kapina udalibe njhalu ni tidakupacha njhalu? 39 Liti mumadwala kapina mwamangidwa mndende tidakuyendelani?40 Mfumu siwaayanghe, Zene nikukambilani, umo mwamchitila mmojhi wa anyiyawa abale wanga yawo sajhikoza, mwanichitila ine!"

Veja também