59 Ndiipo Yusufu wadatenga chitanda cha Yesu ni kuchiveka sanda, 60 wadachiika chitanda muchiliza chake cha chipano icho wadakumba mundhaka yolimba. Ndiipo wadauvilingicha mwala waukulu pakhomo la chiliza ni kuchokapo.
59 Ndiipo Yusufu wadatenga chitanda cha Yesu ni kuchiveka sanda, 60 wadachiika chitanda muchiliza chake cha chipano icho wadakumba mundhaka yolimba. Ndiipo wadauvilingicha mwala waukulu pakhomo la chiliza ni kuchokapo.