Pular para o conteúdo
Publicidade

Mateus 3

Yohane Mbatizi walalikila wandhu

1 Pambuyo pa masiku yambili kupita Yohana Mbatizi wadajha ni kuyamba kulalikila wandhu kuphululu la kujhiko la Yudea niwakamba, 2 "Lapani pakuti ufumu wa kumwamba wawandikila!" 3 Uyu nde Yohana yujha nghani zake zidakambidwa ni mlosi Isaya kuti,

"Mundhu watana ku phululu,

Akonjeleni Ambuye njila yao

tambasulani njila yake!"

4 Yohana wadavala njhalu izo zidakonjedwa ni mabweya ya ngamila ni lamba la chikwetu mchiuno mwake. Chakudya chake chidali nzige ni uchi wa mthengo. 5 Wandhu adafika kwa iye kuchokela kumujhi wa Yelusalemu ni kuchokela madela yonjhe ya kujhiko la Yudea ni mbhepete mwa mchinje Yolodani. 6 Adayavomela machimo yawo ni kuyasiya ni kuwabatiza pa mchinje Yolodani.

Veja também