Pular para o conteúdo
Publicidade

Matayo 15

3 Yesu wadaayangha, "Ndande yanji namwenjho simuchata thauko la Mnungu nambho mchata mayaluzo yanu? 4 Mnungu wakamba, Waalemekeze atate wako ni maye wakoni Waliyonjhe uyo waatukwana atate wake kapina maye wake, waphedwe.5 Nambho anyiimwe muyaluza kuti ngati mundhu wali ni chindhu chalichonjhe icho wakhoza kwathangatila atate wake kapina amaye, nambho wakamba, Chindhu ichi namchochela Mnungu,6 anyiimwe muyaluza mundhu mmeneyo siwafunika kwaalemekeza atate wake ni amake. Chimwecho nde umo mulidelela mawu la Mnungu kwa kuchata mayaluzo yanu mwachinawene wake. 7 Agunghuli anyiimwe! Mlosi Isaya wadalosela bwino nghani zanu, yapo wadakamba kuusu anyiimwe,

8 Mnungu wakamba kuti wandhu anyiyawa anilemekeza kwa maupe,

nambho mmitima mwao alipatali ni ine.

9 Kunilambila kwao kulibe mate,

pakuti ayaluza mayaluzo ya wandhu ngati mayaluzo yanga!"

Veja também