Pular para o conteúdo
Publicidade

Luka 1

28 Mtumiki wa kumwamba wa Mnungu wadamchokela ni kumlonjela ni kumkambila, "Iwe wapachidwa mwawi, Ambuye ali pamojhi ni iwe!" 29 Maliya yapo wadavela moni imeneyo wadaiganizila kupunda niwadakamba kuti moni iyi mate yake chiyani. 30 Nambho mtumiki wa kumwamba wa Mnungu wadamkambila, "Maliya usadaopa, pakuti Mnungu wakupacha mwawi. 31 Vechela, siupate pathupi ni kubala mwana wa mmuna, niiwe siumpache jhina Yesu.

Veja também