Publicidade

Salmos 103

1 Tamanda Yehova, iwe moyo wanga;

ndi zonse zamʼkati mwanga zitamande dzina lake loyera.

2 Tamanda Yehova, iwe moyo wanga,

ndipo usayiwale zabwino zake zonse.

3 Amene amakhululuka machimo ako onse

ndi kuchiritsa nthenda zako zonse,

4 amene awombola moyo wako ku dzenje

ndi kukuveka chikondi ndi chifundo chake ngati chipewa chaufumu,

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-22_10-02-25-