Pular para o conteúdo
Publicidade

Salmos 119

9 Kodi mnyamata angathe bwanji kuyeretsa mayendedwe ake?

Akawasamala potsata mawu anu.

10 Ndimakufunafunani ndi mtima wanga wonse;

musalole kuti ndisochere kuchoka pa malamulo anu.

11 Ndasunga mawu anu mu mtima mwanga

kuti ndisakuchimwireni.

Veja também