Pular para o conteúdo
Publicidade

MASALIMO 127

3 Ana ndiye cholowa chochokera kwa Yehova,

ana ndi mphotho yochokera kwa Iye.

4 Ana a pa unyamata ali ngati mivi mʼmanja

mwa munthu wankhondo.

5 Wodala munthu

amene motengera mivi mwake mwadzaza.

Iwo sadzachititsidwa manyazi

pamene alimbana ndi adani awo pa zipata.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também