Pular para o conteúdo
Publicidade

Salmos 139

1 Inu Yehova, mwandisanthula

ndipo mukundidziwa.

2 Inu mumadziwa pamene ndikhala pansi ndi pamene ndidzuka;

mumazindikira maganizo anga muli kutali.

3 Mumapenyetsetsa pamene ndikutuluka ndi kugona kwanga;

mumadziwa njira zanga zonse.

4 Mawu asanatuluke pa lilime langa

mumawadziwa bwinobwino, Inu Yehova.

Veja também