Pular para o conteúdo
Publicidade

MASALIMO 146

1 Tamandani Yehova.

Tamanda Yehova, iwe moyo wanga.

2 Ndidzatamanda Yehova ndi moyo wanga wonse;

ndidzayimba nyimbo zamatamando kwa Mulungu wanga nthawi yonse ya moyo wanga.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também