Pular para o conteúdo
Publicidade

MASALIMO 22

16 Agalu andizungulira;

gulu la anthu oyipa landizinga.

Alasa manja ndi mapazi anga.

17 Ine nditha kuwerenga mafupa anga onse;

anthu amandiyangʼanitsitsa ndi kundidzuma.

18 Iwo agawana zovala zanga pakati pawo

ndi kuchita maere pa zovala zangazo.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também