Pular para o conteúdo
Publicidade

Salmos 23

1 Yehova ndiye mʼbusa wanga, sindidzasowa kanthu.

2 Amandigoneka pa msipu wobiriwira,

amanditsogolera ku madzi akumwa abwino,

3 amatsitsimutsa moyo wanga.

Amanditsogolera mʼnjira zachilungamo

chifukwa cha dzina lake.

Veja também