Pular para o conteúdo
Publicidade

Salmos 24

1 Dziko lapansi ndi la Yehova ndi zonse zimene zili mʼmenemo,

dziko ndi onse amene amakhala mʼmenemo;

2 pakuti Iye ndiye anayika maziko ake pa nyanja

ndi kulikhazika pamwamba pa madzi.

Veja também