Publicidade

Salmos 24

3 Ndani angakwere phiri la Yehova?

Ndani angathe kuyima pa malo ake opatulika?

4 Iye amene ali ndi mʼmanja moyera ndi mtima woyera,

amene sapereka moyo wake kwa fano

kapena kulumbira mwachinyengo.

5 Iyeyo adzalandira madalitso kwa Yehova

ndipo Mulungu mpulumutsi wake adzagamula kuti alibe mlandu.

Veja também

Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-07-05_12-11-46-