Pular para o conteúdo
Publicidade

MASALIMO 30

4 Imbirani Yehova inu anthu ake okhulupirika;

tamandani dzina lake loyera.

5 Pakuti mkwiyo wake umakhala kwa kanthawi

koma kukoma mtima kwake ndi kwa moyo wonse;

utha kuchezera kulira usiku wonse,

koma chimwemwe chimabwera mmawa.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também