23 Ngati Yehova akondwera ndi njira ya munthu,
amakhazikitsa mayendedwe ake;
24 ngakhale atapunthwa sadzagwa,
pakuti Yehova amamutchinjiriza ndi dzanja lake.
23 Ngati Yehova akondwera ndi njira ya munthu,
amakhazikitsa mayendedwe ake;
24 ngakhale atapunthwa sadzagwa,
pakuti Yehova amamutchinjiriza ndi dzanja lake.