Pular para o conteúdo
Publicidade

Salmos 37

3 Khulupirira Yehova ndipo uzichita zabwino;

khazikika mʼdziko ndi kutsata zokhulupirika.

4 Udzikondweretse wekha mwa Yehova

ndipo Iye adzakupatsa zokhumba za mtima wako.

5 Pereka njira yako kwa Yehova;

dalira Iye ndipo Iyeyo adzachita izi:

6 Iye adzachititsa chilungamo chako kuwala ngati mʼbandakucha,

chiweruzo chako ngati dzuwa la masana.

Veja também