Publicidade

Salmos 44

6 Sindidalira uta wanga,

lupanga langa silindibweretsera chigonjetso;

7 koma Inu mumatigonjetsera adani athu,

mumachititsa manyazi amene amadana nafe.

8 Timanyadira mwa Mulungu wathu tsiku lonse,

ndipo tidzatamanda dzina lanu kwamuyaya.

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-22_10-02-25-