Pular para o conteúdo
Publicidade

Salmos 51

2 Munditsuke zolakwa zanga zonse

ndipo mundiyeretse kuchotsa tchimo langa.

3 Pakuti ndikudziwa mphulupulu zanga,

ndipo tchimo langa lili pamaso panga nthawi zonse.

4 Motsutsana ndi Inu, Inu nokha, ndachimwa

ndipo ndachita zoyipa pamaso panu,

Kotero kuti inu mwapezeka kuti ndinu wolungama

pamene muyankhula ndi pamene muweruza.

Veja também