Publicidade

Salmos 59

16 Koma ine ndidzayimba za mphamvu yanu,

mmawa ndidzayimba zachikondi chanu;

pakuti ndinu linga langa,

pothawirapo panga mʼnthawi ya mavuto.

17 Inu mphamvu yanga, ndiyimba matamando kwa inu;

Inu Mulungu, ndinu linga langa, Mulungu wanga wachikondi.

Veja também

Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-07-05_12-11-46-