Publicidade

Salmos 65

1 Matamando akudikira Inu Mulungu mu Ziyoni;

kwa inu malumbiro athu adzakwaniritsidwa.

2 Inu amene mumamva pemphero,

kwa inu anthu onse adzafika.

3 Pamene tinathedwa nzeru ndi machimo,

Inu munakhululukira mphulupulu zathu.

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-22_10-02-25-