23 Komabe Iye anapereka lamulo kwa mitambo mmwamba
ndi kutsekula makomo a mayiko akumwamba;
24 anagwetsa mana kuti anthu adye,
anawapatsa tirigu wakumwamba.
25 Anthu anadya buledi wa angelo,
Iye anawatumizira chakudya chonse chimene akanatha kudya.
23 Komabe Iye anapereka lamulo kwa mitambo mmwamba
ndi kutsekula makomo a mayiko akumwamba;
24 anagwetsa mana kuti anthu adye,
anawapatsa tirigu wakumwamba.
25 Anthu anadya buledi wa angelo,
Iye anawatumizira chakudya chonse chimene akanatha kudya.