Pular para o conteúdo
Publicidade

Salmos 78

23 Komabe Iye anapereka lamulo kwa mitambo mmwamba

ndi kutsekula makomo a mayiko akumwamba;

24 anagwetsa mana kuti anthu adye,

anawapatsa tirigu wakumwamba.

25 Anthu anadya buledi wa angelo,

Iye anawatumizira chakudya chonse chimene akanatha kudya.

Veja também