Pular para o conteúdo
Publicidade

MASALIMO 78

23 Komabe Iye anapereka lamulo kwa mitambo mmwamba

ndi kutsekula makomo a mayiko akumwamba;

24 anagwetsa mana kuti anthu adye,

anawapatsa tirigu wakumwamba.

25 Anthu anadya buledi wa angelo,

Iye anawatumizira chakudya chonse chimene akanatha kudya.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também