Pular para o conteúdo
Publicidade

MASALIMO 119

97 Ndithu, ine ndimakonda malamulo anu!

Ndimalingaliramo tsiku lonse.

98 Malamulo anu amachititsa kuti ndikhale wanzeru kuposa adani anga,

popeza malamulowo ali ndi ine nthawi zonse.

99 Ndimamvetsa zinthu kwambiri kuposa aphunzitsi anga onse

popeza ndimalingalira umboni wanu.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também