Pular para o conteúdo
Publicidade

Salmos 126

5 Iwo amene amafesa akulira,

adzakolola akuyimba nyimbo zachimwemwe.

6 Iye amene amayendayenda nalira,

atanyamula mbewu yokafesa,

adzabwerera akuyimba nyimbo zachimwemwe,

atanyamula mitolo yake.

Veja também