Publicidade

Salmos 34

1 Ndidzayamika Yehova nthawi zonse;

matamando ake adzakhala pa milomo yanga nthawi zonse.

2 Moyo wanga udzanyadira Yehova;

anthu osautsidwa amve ndi kukondwera.

3 Lemekezani Yehova pamodzi ndi ine;

tiyeni pamodzi tikuze dzina lake.

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-22_10-02-25-