Pular para o conteúdo
Publicidade

MASALIMO 34

12 Aliyense wa inu amene amakonda moyo wake

ndi kukhumba kuti aone masiku abwino ambiri,

13 asunge lilime lake ku zoyipa

ndi milomo yake kuti isayankhule zonama.

14 Tembenuka kuchoka ku zoyipa ndipo chita zabwino;

funafuna mtendere ndi kuwulondola.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também