39 Chipulumutso cha olungama chimachokera kwa Yehova;
Iye ndiye linga lawo pa nthawi ya masautso.
40 Yehova amawathandiza ndi kuwalanditsa;
Iye amawalanditsa kwa oyipa ndi kuwapulumutsa,
pakuti amathawira kwa Iye.
39 Chipulumutso cha olungama chimachokera kwa Yehova;
Iye ndiye linga lawo pa nthawi ya masautso.
40 Yehova amawathandiza ndi kuwalanditsa;
Iye amawalanditsa kwa oyipa ndi kuwapulumutsa,
pakuti amathawira kwa Iye.