Publicidade

Salmos 51

9 Mufulatire machimo anga

ndi kufafaniza zolakwa zanga zonse.

10 Mulenge mʼkati mwanga mtima woyera Inu Mulungu

ndi kukonzanso mzimu wokhazikika mwa ine.

11 Musandichotse pamaso panu

kapena kuchotsa Mzimu wanu Woyera mwa ine.

Veja também

Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-07-05_12-11-46-