4 Mtima wanga ukupweteka mʼkati mwanga;
mantha a imfa andigwera.
5 Mantha ndi kunjenjemera zandizinga;
mantha aakulu andithetsa nzeru.
4 Mtima wanga ukupweteka mʼkati mwanga;
mantha a imfa andigwera.
5 Mantha ndi kunjenjemera zandizinga;
mantha aakulu andithetsa nzeru.
+581 estão orando agora.
Junte-se à corrente de oração.