Publicidade

Salmos 8

3 Pamene ndilingalira za mayiko anu akumwamba,

ntchito ya zala zanu,

mwezi ndi nyenyezi,

zimene mwaziyika pa malo ake,

4 munthu ndani kuti Inu mumamukumbukira,

ndi mwana wa munthu kuti inu mumacheza naye?

5 Inu munamupanga kukhala wocheperapo kusiyana ndi zolengedwa zakumwamba

ndipo mwamuveka ulemerero ndi ulemu.

Veja também

Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-07-05_19-25-13-