7 Yehova akulamulira kwamuyaya;
wakhazikitsa mpando wake waufumu woweruzira.
8 Iye adzaweruza dziko mwachilungamo;
adzalamulira mitundu ya anthu mosakondera.
7 Yehova akulamulira kwamuyaya;
wakhazikitsa mpando wake waufumu woweruzira.
8 Iye adzaweruza dziko mwachilungamo;
adzalamulira mitundu ya anthu mosakondera.